UYU WANENA ZOONA UYU Alice Nankho Banda Am in south africa, am educated Malawian ndugwira ntchito pa Filling station, ndalama timakhala nazo its true musayese ngati timavutikka kuno mayazi. Ena kumudziko mumalamba zoti ife tuvutika mukunama, koma nkhawa zanga zili pa Matenda anthufe tikadwala ndi mavuto ambiri tikumangozifera mmanyumba kuno because sitimakaima nao mu zipatala zakuno unless upite ku clinic or else ungopeza mankhwala umwe ukachira thank God. Vuto zinjoyi kuno sinkhani nde ukaaphwanya man kuti uzilandira ma ARV ndi mbola moti zongofuna kupewa otherwise ena tumamwalira ndi matenda ochizika kuno. Thank you in advance admin #Ahead
Posted on: Sat, 27 Jul 2013 04:19:47 +0000