AbaleTIYENI tipempherere dziko lathu ,becoz the speech of - TopicsExpress



          

AbaleTIYENI tipempherere dziko lathu ,becoz the speech of tanzanian presdent yesterday shows that they döt care about malawi (kuderera malawi) dzulo wanenetsa kuti his army is ready to deal with any country omwe akufuna kuwabera nyanja yawo ,ndipo akaulitsa monga momwe anakhaulitsira idamin ndiziko la uganga 1979,my simple fuso is that kodi akudelera utsogoleri?nthawi ya kamuzu ,Bakiri Bingu zosezi kunalibe tandiyankhani a malawi kenakó pray 4 our country.God bles u all
Posted on: Fri, 26 Jul 2013 04:27:41 +0000

Trending Topics



Recently Viewed Topics




© 2015