IZEKI NDI JAKOBO Ku Malawi kuno mpovuta kuiwala Izeki ndi Jakobo pankhani yanthabwala , komanso ma dramma Du Chisiza Junior ........,......... Chimodzimodzi England isanabwenzeretse William Shakespeare mpakana lero; wolemba mabuku uja. Munthu anamwalira pa 23rd April , 1616 : Koma palibe akumposa , anthu kumangokopera Lero ndionera Izeki ndi Jakobo mpakana tchwelofu usiku motere : 1. Padepoti 2. Alonda 3. Amu ze rodi yu woko 4. Yonamizira maliro 5. Yochekera wansembe palilaka 6. Yoweta nkhumba 7. Atelara 8 .Yangongole 9. Mntengo ku sitediyamu 10. Ulendo waku Dallas {America } 11 .Yobwerekana bokosi lamaliro 12.Njinga Osamangoti kuli Mr Bean , Clint the Drunk , Charlie Chaplain , Basketmouth , Shucks Shabalala . Zacizungu ! pena chikupitepo koma umangosekabe or sunamve nkomwe............,.............
Posted on: Thu, 25 Sep 2014 11:49:07 +0000