NAMBEWE: Nyamaji? Bwera ujapase alendo moni. NYAMAJI: Muli bwanji - TopicsExpress



          

NAMBEWE: Nyamaji? Bwera ujapase alendo moni. NYAMAJI: Muli bwanji alendo? ALENDO: Ndili pyadidi penumbo iwe? NYAMAJI: Ati ndimwe alendo? Kwanu ndi kupi? ALENDO: Ndabukira kwa mbenje. NAMBEWE: Aaaah iwe Nyamaji, usaphatephate anthu tepo tai unaaswipisa. ALENDO: Msiyeni pyache ndi mwana. NYAMAJI: Pyabwelemwe tepa lero munenda kwanu lini? ALENDO: Nenda mangwana. NYAMAJI: Ife lero tinadya na muliwo wa nkhuku, imwe munadyambo? NAMBEWE: Nyamaji, Nyamaji nakumenya ine iwe? Ndoko kasenjeke kunaanjako uko.
Posted on: Mon, 07 Oct 2013 03:44:45 +0000

Trending Topics



Recently Viewed Topics




© 2015