Anthu omwe munathawa ku Malawi kupita ku mayiko ena mwanyanya kunyoza ku malawi, ngati mukufuna kuti zinthu zisithe pitani konko ku malawi mukathandizane ndi aboma wo than kumangochita update ma status anu ochita compare malawi ndi ku magalande komwe muliko, isaaaaaaa mwaonjeza inu phwiii kukhalira facebook azanu ali ku malawi akuyesayesa kusitha zinthu, chete matchona nose tamangochitani za azungu anuwo!!!!
Posted on: Tue, 07 Oct 2014 17:40:01 +0000
Trending Topics
Recently Viewed Topics
© 2015